Genesis 5:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Atabadwa Seti, Adamu anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Masiku ake Adamu atabala Seti, anali zaka mazana asanu ndi atatu; ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Masiku ake Adamu atabala Seti, anali zaka mazana asanu ndi atatu; ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pambuyo pake Adamu adakhala ndi moyo zaka zinanso 800. Adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi. Onani mutuwo |