Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 3:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mkaziyo anati kwa njokayo, “Tikhoza kudya zipatso za mʼmitengo ya mʼmundawu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Mkaziyo ndipo anati kwa njoka, Zipatso za mitengo ya m'mundamu tidye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Mkaziyo ndipo anati kwa njoka, Zipatso za mitengo ya m'mundamu tidye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mkazi uja adayankha kuti, “Tingathe kudya zipatso za mtengo uliwonse m'munda muno,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 3:2
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova Mulungu analamula munthu uja kuti, “Uzidya zipatso za mu mtengo wina uliwonse mʼmundamu;


koma usadye zipatso za mu mtengo wodziwitsa chabwino ndi choyipa, popeza ukadzadya za mu mtengowu udzafa ndithu.”


koma Mulungu anati, ‘Musadye zipatso za mu mtengo umene uli pakati pa munda, ndipo musadzawukhudze kuti mungadzafe.’ ”


Ululu wawo uli ngati ululu wa njoka, ngati uja wa mphiri imene yatseka mʼmakutu mwake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa