Genesis 13:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 ndiponso kumene Abramu anamangira Yehova guwa lansembe kwa nthawi yoyamba ndi kupemphera mʼdzina la Yehova. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 kumalo kwa guwa la nsembe analimanga iye kumeneko, poyamba paja; ndipo pamenepo Abramu anaitanira dzina la Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 kumalo kwa guwa la nsembe analimanga iye kumeneko, poyamba paja; ndipo pamenepo Abramu anaitanira dzina la Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono adabwereranso ku malo aja kumene kale adaamangako guwa, ndipo adatama dzina la Chauta mopemba. Onani mutuwo |