Genesis 10:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Ndi ana aamuna a Yavani: Elisa, ndi Tarisisi, ndi Kitimu, ndi Dodanimu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndi ana amuna a Yavani: Elisa, ndi Tarisisi, ndi Kitimu, ndi Dodanimu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ana a Yavani anali Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Dodanimu. Onani mutuwo |