Genesis 1:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo Mulungu anapanga thambo nalekanitsa madzi amene anali pansi ndi pamwamba pa thambo lija, ndipo zinachitikadi. Onani mutuwoBuku Lopatulika7 Ndipo Mulungu anapanga thambo, nalekanitsa madzi anali pansi pathambolo ndi madzi anali pamwamba pathambolo; ndipo kunatero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Mulungu anapanga thambo, nalekanitsa madzi anali pansi pa thambolo ndi madzi anali pamwamba pa thambolo; ndipo kunatero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Motero Mulungu adalenga cholekanitsa madzi chija, naŵagaŵa madziwo, ena pansi pa cholekanitsacho ena pamwamba pake. Onani mutuwo |