Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Filemoni 1:24 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Atumiki anzanga awa, Marko, Aristariko, Dema ndi Luka, akuperekanso moni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

24 ateronso, Marko, Aristariko, Dema, Luka, antchito anzanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 ateronso, Marko, Aristariko, Dema, Luka, antchito anzanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Akutinso moni anzanga antchito, Marko, Aristariko, Dema, ndi Luka.

Onani mutuwo Koperani




Filemoni 1:24
15 Mawu Ofanana  

Atazindikira zimenezi anapita ku nyumba ya Mariya amayi ake a Yohane, wotchedwanso Marko, kumene kunasonkhana anthu ambiri ndipo amapemphera.


Barnaba ndi Saulo atamaliza ntchito yawo anachoka ku Yerusalemu, atatenga Yohane wotchedwanso Marko.


Kuchokera ku Pafo, Paulo ndi anzake anayenda pa sitima ya pamadzi kupita ku Perga wa ku Pamfiliya, kumeneko Yohane anawasiya nabwerera ku Yerusalemu.


Nthawi yomweyo mu mzinda wonse munabuka chipolowe. Anthu anagwira Gayo ndi Aristariko, anzake a Paulo a ku Makedoniya, ndipo anathamangira nawo ku bwalo la masewero.


Tinakwera sitima ya pamadzi yochokera ku Adramutiyo imene inali yokonzeka kale kupita ku madooko a ku Asiya, ndipo tinanyamuka. Aristariko, wa ku Makedoniya wa ku mzinda wa Tesalonika, anali nafe.


Kunena za Tito, ndiye mnzanga ndi wogwira naye ntchito pakati panu. Kunena za abale athu, ndiwo oyimirira mipingo ndi olemekezetsa Khristu.


Koma ndikuganiza kuti nʼkofunika kuti ndikutumizireni mʼbale wanga Epafrodito, mtumiki mnzanga ndi msilikali mnzanga, amenenso ndi mtumiki wanu amene munamutumiza kuti adzandithandize pa zosowa zanga.


Inde, ndikupempha iwe mnzanga pa ntchitoyi, thandiza amayiwa amene ndagwira nawo ntchito ya Uthenga Wabwino pamodzi ndi Klementonso ndi ena onse antchito anzanga amene mayina awo ali mʼbuku lamoyo.


Aristariko, wamʼndende mnzanga akupereka moni, Marko akuperekanso moni, msuweni wa Barnaba. (Inu munawuzidwa kale za Iye. Iye akabwera kwanuko, mulandireni).


Luka, dotolo wathu wokondedwa ndi Dema, akupereka moni.


Imani mwamphamvu mʼchisomochi. Mlongo wanu amene ali ku Babuloni, wosankhidwa pamodzi nanu akupereka moni, nayenso Marko, mwana wanga, akupereka moni.


Ife tiyenera kumathandiza anthu oterewa, kuti tigwirizane nawo pa ntchito ya choonadi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa