Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Filemoni 1:23 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Epafra, wamʼndende mnzanga chifukwa cha Khristu Yesu akupereka moni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

23 Epafra wandende mnzanga mwa Khristu Yesu akukupatsa moni;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Epafra wandende mnzanga mwa Khristu Yesu akukupatsa moni;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Akukupatsa moni Epafra, amene ali m'ndende pamodzi nane chifukwa cha Khristu Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Filemoni 1:23
6 Mawu Ofanana  

Perekani moni kwa Androniko ndi Yuniya abale anga amene anali mʼndende pamodzi ndi ine. Iwo amadziwika ndi atumwi, ndipo iwo anali mwa Khristu ine ndisanakhale.


Inu munaphunzira zimenezi kuchokera kwa Epafra, mtumiki mnzathu wokondedwa, amene ndi mtumiki wokhulupirika wa Khristu mʼmalo mwathu.


Aristariko, wamʼndende mnzanga akupereka moni, Marko akuperekanso moni, msuweni wa Barnaba. (Inu munawuzidwa kale za Iye. Iye akabwera kwanuko, mulandireni).


Epafra ndi mmodzi mwa inu ndiponso mtumiki wa Khristu Yesu, akupereka moni. Iyeyu nthawi zonse amakupemphererani mwamphamvu, kuti mukhazikike pa chifuniro chonse cha Mulungu, mukhale okhwima ndi otsimikiza kwathunthu.


Kuchokera kwa Paulo, amene ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu ndi Timoteyo mʼbale wathu. Kulembera Filemoni, bwenzi lathu lokondedwa ndi mtumiki mnzathu.


komabe ndikupempha mwachikondi. Ine Paulo, munthu wokalamba, ndipo tsopano ndili mʼndende chifukwa cha Khristu Yesu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa