Eksodo 9:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Koma Yehova anawumitsa mtima wa Farao ndipo iye sanamvere Mose ndi Aaroni monga momwe Yehova anamuwuzira Mose. Onani mutuwoBuku Lopatulika12 Koma Yehova analimbitsa mtima wa Farao, kuti sanamvere iwo; monga Yehova adalankhula ndi Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma Yehova analimbitsa mtima wa Farao, kuti sanamvere iwo; monga Yehova adalankhula ndi Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Koma Mulungu adamuumitsa mtima Farao, ndipo Faraoyo sadaŵalole anthuwo kuti apite monga momwe Chauta adaauzira Mose muja. Onani mutuwo |