Eksodo 8:14 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Aigupto anawunjika achulewo milumilu ndipo dziko linanunkha. Onani mutuwoBuku Lopatulika14 Ndipo anawaola miulumiulu; ndi dziko linanunkha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo anawaola miulumiulu; ndi dziko linanunkha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Aejipito aja adaŵaunjika achulewo milumilu, ndipo dziko lonse lidadzaza ndi chivunde chokhachokha. Onani mutuwo |
“Ine ndidzachotsa ankhondo akumpoto kuti apite kutali ndi inu, kuwapirikitsira ku dziko lowuma ndi lachipululu, gulu lawo lakutsogolo ndidzalipirikitsira ku nyanja ya kummawa ndi gulu lawo lakumbuyo, ku nyanja ya kumadzulo. Ndipo mitembo yawo idzawola, fungo lake lidzamveka.” Zoonadi Yehova wachita zinthu zazikulu.