Eksodo 8:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mose ndi Aaroni anachoka, ndipo Mose anapemphera kwa Yehova kuti achotse achule amene anatumiza kwa Farao. Onani mutuwoBuku Lopatulika12 Ndipo Mose ndi Aroni anatuluka kwa Farao; ndi Mose anafuulira kwa Yehova kunena za achule amene adawaika pa Farao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Mose ndi Aroni anatuluka kwa Farao; ndi Mose anafuulira kwa Yehova kunena za achule amene adawaika pa Farao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pamenepo Mose ndi Aroni adachoka kwa Farao kuja, ndipo adakapempha Chauta kuti achotse achule amene adaatumiza kwa Farao aja. Onani mutuwo |