Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 7:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Mose ndi Aaroni anachita monga momwe Yehova anawalamulira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Ndipo Mose ndi Aroni anachita monga Yehova anawalamulira, momwemo anachita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Mose ndi Aroni anachita monga Yehova anawalamulira, momwemo anachita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Ndipo Mose ndi Aroni adachitadi zomwe Chauta adaŵalamulazo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 7:6
12 Mawu Ofanana  

ndipo kudzera mwa chidzukulu chako, mitundu yonse ya anthu pa dziko lapansi idzadalitsika, chifukwa iwe wandimvera.”


Nowa anachita zonse monga Mulungu anamulamulira.


Ndipo Nowa anachita zonse zimene Yehova anamulamulira.


Inu mwapereka malangizo ndipo ayenera kutsatidwa kwathunthu.


Aisraeli anachita monga momwe Yehova analamulira Mose ndi Aaroni.


Mose anayendera ntchitoyo ndipo anaona kuti anayichita monga momwe Yehova analamulira. Kotero Mose anawadalitsa.


Mose anachita zonse monga Yehova anamulamulira.


Kotero Mose ndi Aaroni anapita kwa Farao ndi kuchita monga momwe Yehova anawalamulira. Aaroni anaponya ndodo yake pansi patsogolo pa Farao ndi nduna zake ndipo inasanduka njoka.


Iwe ukanene zonse zimene ndakulamulirazi, ndipo Aaroni mʼbale wako ndiye akaziyankhule kwa Farao kuti atulutse ana a Israeli mʼdziko la Igupto.


Mose ndi Aaroni anachita monga momwe Yehova analamulira. Anakweza ndodo yake pamaso pa Farao ndi akuluakulu ake ndipo anamenya madzi a mu Nailo, ndipo madzi onse anasanduka magazi.


Ngati mumvera malamulo anga, mudzakhala mʼchikondi changa, monga Ine ndimamvera malamulo a Atate anga, ndipo ndimakhala mʼchikondi chawo.


Inu ndinu abwenzi anga ngati muchita zimene Ine ndikulamulani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa