Eksodo 7:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mose ndi Aaroni anachita monga momwe Yehova anawalamulira. Onani mutuwoBuku Lopatulika6 Ndipo Mose ndi Aroni anachita monga Yehova anawalamulira, momwemo anachita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Mose ndi Aroni anachita monga Yehova anawalamulira, momwemo anachita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo Mose ndi Aroni adachitadi zomwe Chauta adaŵalamulazo. Onani mutuwo |