Eksodo 7:23 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Mʼmalo mwake iye anatembenuka ndi kupita ku nyumba yake yaufumu ndipo zimenezi sanazilabadire. Onani mutuwoBuku Lopatulika23 Ndipo Farao anatembenuka, nalowa m'nyumba yake, osasamalira ichi chomwe mumtima mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Farao anatembenuka, nalowa m'nyumba yake, osasamalira ichi chomwe mumtima mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pompo Farao adapotoloka, napita kunyumba kwake osalabadanso zimenezo. Onani mutuwo |