Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 7:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Aliyense wa iwo anaponya ndodo yake pansi ndipo inasanduka njoka. Koma ndodo ya Aaroni inameza ndodo zawo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Pakuti yense anaponya pansi ndodo yake, ndipo zinasanduka zinjoka; koma ndodo ya Aroni inameza ndodo zao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Pakuti yense anaponya pansi ndodo yake, ndipo zinasanduka zinjoka; koma ndodo ya Aroni inameza ndodo zao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Adaponyanso pansi ndodo zao, ndipo zidasanduka njoka. Koma ndodo ya Aroni ija idameza ndodo zaozo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 7:12
9 Mawu Ofanana  

Naye Farao anayitanitsa anthu ake anzeru ndi amatsenga, ndipo nawonso amatsenga a Chiigupto anachita zinthu zomwezo mwa matsenga awo.


Koma mtima wa Farao unawuma ndipo sanawamvere monga momwe Yehova ananenera.


Amatsenga sanathe kumuyandikira Mose chifukwa nawonso anali ndi zithupsa monga mmene analili Aigupto ena onse.


Koma sadzapita nazo patali kwambiri zimenezi, pakuti anthu onse adzaona kupusa kwawo monga anachitira Yanesi ndi Yambere.


Inu ana okondedwa, ndinu ochokera kwa Mulungu ndipo mwawagonjetsa aneneri onyengawa, chifukwa Iye amene ali mwa inu ndi wamkulu kuposa amene ali mʼdziko lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa