Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 40:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Kenaka Yehova anati kwa Mose,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tsono Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 40:1
7 Mawu Ofanana  

Tenti ya Yehova imene Mose anapanga mʼchipululu, ndi guwa lansembe zopsereza pa nthawi imeneyi zinali pa phiri ku Gibiyoni.


Kupanga tenti ya msonkhano, bokosi laumboni pamodzi ndi chophimbira chake, ndiponso zonse za mu tenti,


“Anthu onse aluso pakati panu abwere ndi kupanga zonse zimene Yehova walamula:


Tsopano ntchito yonse ya tenti ya msonkhano inatha. Aisraeli anachita zonse monga momwe Yehova analamulira Mose.


Mose anayendera ntchitoyo ndipo anaona kuti anayichita monga momwe Yehova analamulira. Kotero Mose anawadalitsa.


Kotero anayimika chihema tsiku loyamba la mwezi woyamba mʼchaka chachiwiri.


“Imika chihema, tenti ya msonkhano, tsiku loyamba la mwezi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa