Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 38:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Anapanga nyanga imodziimodzi pa ngodya zake zinayizo, kotero kuti nyangazo ndi guwalo zinali chinthu chimodzi, ndipo anakuta guwalo ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Ndipo anapanga nyanga zake pangodya zake zinai; nyanga zake zinakhala zotuluka m'mwemo; ndipo analikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anapanga nyanga zake pangodya zake zinai; nyanga zake zinakhala zotuluka m'mwemo; ndipo analikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Pa ngodya zake zinai adapangapo nyanga zotuluka m'guwalo, mwakuti zidangolumikizika nkukhala chinthu chimodzi ndi guwalo. Ndipo guwa lonselo adalikuta ndi mkuŵa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:2
4 Mawu Ofanana  

Kodi ine ndili ndi mphamvu? Nanga thupi langa ndi lolimba ngati chitsulo?


Upange nyanga imodziimodzi pa ngodya zake zinayizo kuti nyangazo ndi guwalo zikhale chinthu chimodzi, ndipo ulikute guwalo ndi mkuwa.


Anapanga guwa lansembe zopsereza lamatabwa amtengo wa mkesha. Linali lofanana mbali zonse. Msinkhu wake masentimita 137, mulitali mwake masentimita 229, mulifupi masentimita 229.


Anapanganso ziwiya zamkuwa izi zogwirira ntchito pa guwalo: miphika, mafosholo, mabeseni owazira magazi, ngowe zokowera nyama ndi zosonkhezera moto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa