Eksodo 30:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Upange guwa lamatabwa amtengo wa mkesha lofukizirapo lubani. Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Ndipo upange guwa la nsembe la kufukizapo; ulipange la mtengo wakasiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo upange guwa la nsembe la kufukizapo; ulipange la mtengo wakasiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Tsono upange guwa lofukizirapo lubani. Upange guwalo ndi matabwa a mtengo wa kasiya. Onani mutuwo |