Eksodo 3:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mulungu anati, “Ine ndine Mulungu wa makolo ako, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isake, ndi Mulungu wa Yakobo.” Atamva zimenezi, Mose anaphimba nkhope yake chifukwa anaopa kuona Mulungu. Onani mutuwoBuku Lopatulika6 Ananenanso, Ine ndine Mulungu wa atate wako, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo. Ndipo Mose anabisa nkhope yake; popeza anaopa kuyang'ana Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ananenanso, Ine ndine Mulungu wa atate wako, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo. Ndipo Mose anabisa nkhope yake; popeza anaopa kuyang'ana Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adapitirira kunena kuti, “Ine ndine Mulungu wa makolo ako, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, Mulungu wa Yakobe.” Pompo Mose adadziphimba kumaso chifukwa adaopa kupenya Mulungu. Onani mutuwo |