Eksodo 3:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma Mose anafunsa Mulungu, “Ine ndine yani kuti ndipite kwa Farao ndi kukatulutsa Aisraeli mʼdziko la Igupto?” Onani mutuwoBuku Lopatulika11 Koma Mose anati kwa Mulungu Ndine yani ine kuti ndipite kwa Farao, ndi kuti nditulutse ana a Israele mu Ejipito? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma Mose anati kwa Mulungu Ndine yani ine kuti ndipite kwa Farao, ndi kuti nditulutse ana a Israele m'Ejipito? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Apo Mose adafunsa kuti, “Kodi ndine yani ine, kuti ndingapite kwa Farao ndi kukatulutsa Aisraele ku Ejipito?” Onani mutuwo |