Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 27:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Guwalo likhale lamatabwa ndi logoba mʼkati mwake. Ulipange monga momwe ndinakuonetsera pa phiri paja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

8 Ulipange lagweregwere ndi matabwa; monga anakuonetsa m'phirimo; alipange momwemo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ulipange lagweregwere ndi matabwa; monga anakuonetsa m'phirimo; alipange momwemo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ndipo guwalo udzalipange mogoba m'kati mwake. Ulipange monga momwe ndikukulangizira paphiri pano.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 27:8
9 Mawu Ofanana  

Kotero Davide anapatsa Solomoni mwana wake mapulani a khonde la Nyumba ya Mulungu, nyumba zake, mosungiramo katundu, zipinda zake zamʼmwamba, zipinda zamʼkati ndi malo a nsembe zopepesera machimo.


Davide anati, “Zonsezi ndalemba kuchokera kwa Yehova, ndipo Iye wachita kuti ndimvetsetse zonse za mapulaniwa.”


Uwonetsetse kuti wapanga zonse monga momwe ndikukuonetsera pa phiri pano.”


Umange chihema ndiponso ziwiya zamʼkatimo monga momwe Ine ndidzakuonetsere.


Amandilambira Ine kwachabe ndi kuphunzitsa malamulo ndi malangizo a anthu.’ ”


“Makolo athu anali ndi tenti ya msonkhano pakati pawo mʼchipululu. Anayipanga monga momwe Mulungu anawuzira Mose, molingana ndi chithunzi chimene Mose anachiona.


Iwo amatumikira pamalo opatulika amene ndi chithunzi ndi chifanizo cha zimene zili kumwamba. Ichi ndi chifukwa chake Mose anachenjezedwa pamene anali pafupi kumanga Tenti: “Uwonetsetse kuti wapanga zonse monga momwe ndikukuonetsera pa phiri pano.”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa