Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 27:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 “Mbali yakumadzulo ya bwalolo ikhale yotalika mamita 23 ndipo ikhale ndi nsalu yotchinga, nsichi khumi ndi matsinde khumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Ndipo m'kupingasa kwa bwaloli pa mbali ya kumadzulo mukhale nsalu zotchingira za mikono makumi asanu; nsichi zake zikhale khumi, ndi makamwa ao khumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo m'kupingasa kwa bwaloli pa mbali ya kumadzulo mukhale nsalu zochingira za mikono makumi asanu; nsichi zake zikhale khumi, ndi makamwa ao khumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Muufupi mwake mwa bwalolo cha mbali yakuzambwe, pakhale nsalu zochinga, kutalika kwake mamita 23, ndi nsanamira khumi ndi masinde khumi.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 27:12
4 Mawu Ofanana  

Ndipo upange matsinde 40 asiliva ndipo uwayike pansi pa maferemuwo. Pansi pa feremu iliyonse pakhale matsinde awiri ogwiriziza zolumikizira ziwiri zija.


Mbali yakumpoto ikhalenso yotalika mamita 46 ndipo ikhale ndi nsalu yotchinga. Pakhalenso mizati makumi awiri, matsinde amkuwa makumi awiri, ngowe zasiliva ndi zingwe za mizatiyo.


Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, kutalika kwa bwalo kukhale mamita 23.


ndi makatani wotchinga bwalo, katani ya pa chipata cholowera ku bwalo lozungulira Chihema ndi guwa lansembe, zingwe ndi zonse zokhudzana ndi ntchito yawo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa