Eksodo 20:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Uzisunga tsiku la Sabata kuti likhale lopatulika. Onani mutuwoBuku Lopatulika8 Udzikumbukira tsiku la Sabata, likhale lopatulika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Udzikumbukira tsiku la Sabata, likhale lopatulika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Uzikumbukira tsiku la Sabata, uzilisunga loyera. Onani mutuwo |
Nthawi imeneyo ndinaona anthu a mu Yuda akuponda ndi kufinya mphesa pa tsiku la Sabata. Ena ankawunjika tirigu milumilu ndi kumasenzetsa abulu. Enanso ankabwera ndi vinyo, mphesa, mkuyu ndi katundu wa mitundumitundu ku Yerusalemu pa tsiku la Sabata. Choncho ndinawachenjeza za kugulitsa zakudya pa tsiku la Sabata.