Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 20:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndipo Mulungu anayankhula mawu onse awa nati:

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Ndipo Mulungu ananena mau onse amenewa, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Mulungu ananena mau onse amenewa, nati:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tsono Mulungu adalankhula mau onseŵa, adati,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 20:1
11 Mawu Ofanana  

“Munatsika pa Phiri la Sinai, ndipo munawayankhula kuchokera kumwamba. Munawapatsa malangizo olungama, ziphunzitso zoona ndiponso malamulo abwino.


Ndipo Mose anatsika ndi kukawawuza anthuwo.


“Ine ndine Yehova Mulungu wako amene ndinakutulutsa ku Igupto, mʼdziko la ukapolo.


Iyeyu anali mʼgulu la Aisraeli mʼchipululu pamodzi ndi mngelo amene anamuyankhula pa phiri la Sinai ndiponso makolo athu; ndipo Mose analandira mawu amoyo kuti atipatse ife.


Inu amene munalandira Malamulo amene anaperekedwa ndi angelo ndipo simunawamvere.”


Yehova analemba pa miyala iwiriyo zimene analemba poyamba, Malamulo Khumi amene analengeza kwa inu pa phiri paja, mʼmoto, pa tsiku la msonkhano. Ndipo Yehova anawapereka kwa ine.


Kodi uliponso mtundu wina wa anthu umene unamva mawu a Mulungu akuyankhula kuchokera mʼmoto nʼkukhala ndi moyo monga mwachitira inumu?


Kuchokera kumwamba, Iye anafuna kuti inu mumve mawu ake ndi kuti mukhale osunga mwambo. Pa dziko lapansi anakuonetsani moto waukulu, ndipo inu munamva mawu ake kuchokera mʼmotomo.


Awa ndi malamulo amene Yehova anayankhula ndi mawu okweza kwa gulu lanu lonse pa phiri paja mʼmoto, mtambo ndi mdima woopsa, sanawonjezerepo kanthu. Ndipo anawalemba pa mapale awiri amiyala ndi kundipatsa.


Yehova anayankhula nanu maso ndi maso kuchokera mʼmoto pa phiri paja.


“Ine ndine Yehova Mulungu wako amene ndinakutulutsa ku Igupto, mʼdziko la ukapolo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa