Eksodo 2:22 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Zipora anabereka mwana wa mwamuna amene Mose anamutcha Geresomu, popeza anati, “Ndakhala mlendo mʼdziko la eni.” Onani mutuwoBuku Lopatulika22 Ndipo anaona mwana, ndi Mose anamutcha dzina lake Geresomo; pakuti anati, Ndakhala mlendo m'dziko la eni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo anaona mwana, ndi Mose anamutcha dzina lake Geresomo; pakuti anati, Ndakhala mlendo m'dziko la eni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Zipora adabala mwana wamwamuna. Pamenepo Mose adati, “Ndine mlendo m'dziko lachilendo.” Motero adamutcha mwanayo Geresomo. Onani mutuwo |