Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 2:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Atayangʼana uku ndi uku, naona kuti panalibe wina aliyense, Mose anamupha Mwiguptoyo ndipo anamukwirira mu mchenga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Ndipo anaunguza kwina ndi kwina, ndipo pamene anaona kuti palibe munthu, anakantha Mwejipito, namfotsera mumchenga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo anaunguza kwina ndi kwina, ndipo pamene anaona kuti palibe munthu, anakantha Mwejipito, namfotsera mumchenga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Pamenepo Mose atayang'ana uku ndi uku, naona kuti kulibe anthu, adamupha Mwejipitoyo, nafotsera mtembo wake mu mchenga.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 2:12
1 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa