Eksodo 17:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo Mose anapemphera kwa Yehova, “Kodi ndichite chiyani ndi anthu awa? Iwo atsala pangʼono kundigenda ndi miyala.” Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Ndipo Mose anafuulira kwa Yehova, ndi kuti, Ndiwachitenji anthuwa? Atsala pang'ono kundiponya miyala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Mose anafuulira kwa Yehova, ndi kuti, Ndiwachitenji anthuwa? Andilekera pang'ono kundiponya miyala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Apo Mose adapemphera mokweza mau kwa Chauta, adati, “Kodi anthu ameneŵa ndichite nawo chiyani? Iwowo ngokonzeka kundiponya miyala.” Onani mutuwo |