Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 16:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Mʼchipululumo gulu lonse linadandaulira Mose ndi Aaroni

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Ndipo khamu lonse la ana a Israele linadandaulira Mose ndi Aroni m'chipululu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo khamu lonse la ana a Israele linadandaulira Mose ndi Aroni m'chipululu

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndipo khamu lonse lidadandaulira Mose ndi Aroni m'chipululu muja kuti,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:2
10 Mawu Ofanana  

Alendo aja asanapite kogona, amuna onse achinyamata ndi achikulire ochokera mbali zonse za mzinda wa Sodomu anazinga nyumba ya Loti.


Koma posachedwa anayiwala zimene Iye anachita, ndipo sanayembekezere uphungu wake.


Anangʼungʼudza mʼmatenti mwawo ndipo sanamvere Yehova.


Pamene makolo athu anali mu Igupto, sanalingalire za zozizwitsa zanu; iwo sanakumbukire kukoma mtima kwanu kochuluka, ndipo anawukira Inu pa Nyanja Yofiira.


Iwo anafunsa Mose kuti, “Kodi nʼchifukwa chakuti kunalibe manda ku dziko la Igupto kuti iwe utibweretse muno mʼchipululu kuti tidzafe? Chimene watichitachi nʼchiyani, kutitulutsa mʼdziko la Igupto?


Tsono anthu aja anadandaulira Mose ndi kumufunsa kuti, “Kodi tikumwa chiyani?”


Koma anthu anali ndi ludzu pamenepo ndipo anangʼungʼudza pamaso pa Mose namufunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani unatitulutsa mʼdziko la Igupto kuti ife, ana athu pamodzi ndi ziweto zathu tife ndi ludzu?”


ndipo iwo anati, “Yehova akupenyeni ndi kukuweruzani popeza mwachititsa Farao ndi nduna zake kuti anyansidwe nafe ndipo mwayika lupanga mʼmanja mwawo kuti atiphe.”


palibe ndi mmodzi yemwe mwa anthu amene anaona ulemerero wanga ndi zizindikiro zozizwitsa zimene ndinazichita ku Igupto ndi mʼchipululu muno, koma osandimvera ndi kundiyesa kokwanira kakhumi,


Ndipo osamawiringula, monga ena mwa iwo anachitira naphedwa ndi mngelo wowononga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa