Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 15:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Munatambasula dzanja lanu lamanja ndipo dziko linawameza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Mwatambasula dzanja lanu lamanja, nthaka inawameza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Mwatambasula dzanja lanu lamanja, nthaka inawameza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Mudatambalitsa dzanja lanu lamanja, ndipo nthaka idaŵameza.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 15:12
3 Mawu Ofanana  

Ngakhale ndiyende pakati pa masautso, mumasunga moyo wanga; mumatambasula dzanja lanu kutsutsana ndi mkwiyo wa adani anga, mumandipulumutsa ndi dzanja lanu lamanja.


Yehova, dzanja lanu lamanja ndi laulemerero chifukwa cha mphamvu zake. Ndithu Yehova, dzanja lanu lamanja linaphwanya mdani.


Izi ndizo ndakonza kuti zichitike pa dziko lonse lapansi, ndatambasula dzanja pa anthu a mitundu yonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa