Eksodo 13:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 muzikapereka kwa Ambuye ana onse oyamba kubadwa. Ziweto zonse zazimuna zoyamba kubadwa ndi za Ambuye. Onani mutuwoBuku Lopatulika12 kuti uzikapatulira Yehova onse oyamba kubadwa ndi oyamba onse uli nao odzera kwa zoweta; amunawo ndi a Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 kuti uzikapatulira Yehova onse oyamba kubadwa ndi oyamba onse uli nao odzera kwa zoweta; amunawo ndi a Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 muzidzapereka kwa Chauta chilichonse choyamba kubadwa. Zoŵeta zanu zamphongo zoyamba kubadwa nza Chauta zimenezo. Onani mutuwo |