Eksodo 13:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Muzichita mwambo uwu pa nthawi yake chaka ndi chaka. Onani mutuwoBuku Lopatulika10 Chifukwa chake uzikasunga lemba ili pa nyengo yake chaka ndi chaka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chifukwa chake uzikasunga lemba ili pa nyengo yake chaka ndi chaka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Musunge malangizo ameneŵa pa nthaŵi yake chaka ndi chaka. Onani mutuwo |
“Muzichita Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti. Kwa masiku asanu ndi awiri muzidya buledi wopanda yisiti monga ndinakulamulirani. Muzichita zimenezi mwezi wa Abibu pa nthawi yomwe ndayika, pakuti mʼmwezi umenewu munatuluka mʼdziko la Igupto. “Pasapezeke munthu wobwera pamaso panga wopanda kanthu mʼmanja.