Eksodo 12:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo adzatengeko magazi anyamazo ndi kuwaza pa mphuthu ziwiri za chitseko ndiponso pamwamba pa chitseko cha nyumba mmene adzadyeremo ana ankhosawo. Onani mutuwoBuku Lopatulika7 Ndipo azitengako mwazi, naupake pa mphuthu za mbali ndi ya pamwamba m'nyumba zimene adyeramo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo azitengako mwazi, naupake pa mphuthu za mbali ndi ya pamwamba m'nyumba zimene adyeramo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono adzatengeko magazi a nyamayo ndi kuwaza pa mphuthu ziŵiri za chitsekozo, ndi pamwamba pa chitseko cha nyumba m'mene akadyeremo nyamayo. Onani mutuwo |