Eksodo 12:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Muzisunge mpaka tsiku la khumi ndi chinayi la mwezi, pamene gulu lonse la Aisraeli lidzaphe nyamazo madzulo. Onani mutuwoBuku Lopatulika6 Ndipo mukhale naye chisungire kufikira tsiku lakhumi ndi chinai la mwezi womwe; ndipo gulu lonse la Israele lizamuphe madzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo mukhale naye chisungire kufikira tsiku lakhumi ndi chinai la mwezi womwe; ndipo bungwe lonse la anthu a Israele lizimupha madzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mumsunge mpaka tsiku la 14 la mwezi, pamene khamu lonse la Aisraele lidzaphe nyama zaozo madzulo ndithu. Onani mutuwo |