Eksodo 12:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Mwezi uno uzikhala mwezi wanu woyamba wa chaka. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 Mwezi uno uzikhala kwa inu woyamba wa miyezi; muziuyesa mwezi woyamba wa chaka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mwezi uno uzikhala kwa inu woyamba wa miyezi; muziuyesa mwezi woyamba wa chaka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Mwezi uno udzakhala mwezi wanu woyambira chaka. Onani mutuwo |
“Muzichita Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti. Kwa masiku asanu ndi awiri muzidya buledi wopanda yisiti monga ndinakulamulirani. Muzichita zimenezi mwezi wa Abibu pa nthawi yomwe ndayika, pakuti mʼmwezi umenewu munatuluka mʼdziko la Igupto. “Pasapezeke munthu wobwera pamaso panga wopanda kanthu mʼmanja.