Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 9:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mʼchaka choyamba cha Dariyo mwana wa Ahasiwero (wochokera kwa Amedi), amene anakhala mfumu ya ku Babuloni,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Chaka choyamba cha Dariusi mwana wa Ahasuwero, wa mbeu ya Amedi, amene anamlonga mfumu ya Ababiloni;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Chaka choyamba cha Dariusi mwana wa Ahasuwero, wa mbeu ya Amedi, amene anamlonga mfumu ya Ababiloni;

Onani mutuwo Koperani




Danieli 9:1
9 Mawu Ofanana  

Mfumu Ahasiwero atangoyamba kulamulira dzikolo, adani aja analemba kalata yoneneza anthu a Yuda ndi Yerusalemu.


Izi ndi zimene zinachitika pa nthawi ya ufumu wa Ahasiwero, amene analamulira zigawo 127 kuyambira ku India mpaka ku Kusi.


Ndipo Danieli anali kumeneko mpaka chaka choyamba cha ufumu wa Koresi.


achinyamata wopanda chilema, okongola, aluso mu nzeru zonse, okhala ndi chidziwitso, achangu pophunzira, odziwa kutumikira mʼnyumba ya mfumu. Ndipo anati awaphunzitsenso kuwerenga chiyankhulo cha Ababuloni.


Ndipo chaka choyamba cha Dariyo Mmedi ine Mikayeli ndinabwera kumuthandiza ndi kumuteteza Gabrieli.


ndipo Dariyo Mmedi analanda ufumuwo ali ndi zaka 62.


Kunamukomera Dariyo kusankha akalonga 120 kuti alamulire mu ufumu wonse,


Choncho Danieli anapeza ufulu pa nthawi ya ulamuliro wa Dariyo ndi ulamuliro wa Koresi wa ku Perisiya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa