Danieli 9:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼchaka choyamba cha Dariyo mwana wa Ahasiwero (wochokera kwa Amedi), amene anakhala mfumu ya ku Babuloni, Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Chaka choyamba cha Dariusi mwana wa Ahasuwero, wa mbeu ya Amedi, amene anamlonga mfumu ya Ababiloni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chaka choyamba cha Dariusi mwana wa Ahasuwero, wa mbeu ya Amedi, amene anamlonga mfumu ya Ababiloni; Onani mutuwo |