Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 7:17 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 ‘Zirombo zikuluzikulu zinayi zija ndi maufumu anayi amene adzaoneka pa dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

17 Zilombo zazikulu izi zinai ndizo mafumu anai amene adzauka padziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Zilombo zazikulu izi zinai ndizo mafumu anai amene adzauka pa dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 7:17
9 Mawu Ofanana  

Inu Yehova, pulumutseni ndi dzanja lanu kwa anthu otere, kwa anthu a dziko lino amene mphotho yawo ili mʼmoyo uno. Inu mumaletsa njala kwa amene asangalatsidwa nanu; ana awo aamuna ali ndi zinthu zambiri, ndipo iwo amasunga chuma cha ana awo.


Ndinayandikira mmodzi mwa amene anayima pamenepo ndi kumufunsa tanthauzo lenileni la zonsezi. “Kotero anandiwuza ndi kundipatsa tanthauzo la zinthu zonse izi:


Koma oyera mtima a Wammwambamwamba adzalandira ufumu ndipo udzakhala nawo mpaka muyaya, inde ku nthawi zonse.’


Yesu anati, “Ufumu wanga si wa dziko lapansi lino. Ukanakhala wa pansi pano, antchito anga akanachita nkhondo kulepheretsa Ayuda kundigwira. Koma tsopano ufumu wanga ndi wochokera kumalo ena.”


Ndipo ndinaona chirombo chikutuluka mʼnyanja. Chinali ndi nyanga khumi ndi mitu isanu ndi iwiri. Pa nyanga iliyonse chinavala chipewa chaufumu, ndipo pa mutu uliwonse panali dzina lonyoza Mulungu.


Kenaka ndinaona chirombo china chikutuluka mʼnthaka. Chinali ndi nyanga ziwiri ngati mwana wankhosa koma kuyankhula kwake ngati chinjoka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa