Danieli 5:26 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 “Zimene mawuwa akutanthauza ndi izi: Mene: Mulungu wawerenga masiku a ufumu wanu ndipo wauthetsa. Onani mutuwoBuku Lopatulika26 Kumasulira kwake kwa mau awa ndi uku: MENE, Mulungu anawerenga ufumu wanu, nautha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Kumasulira kwake kwa mau awa ndi uku: MENE, Mulungu anawerenga ufumu wanu, nautha. Onani mutuwo |