Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 5:26 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 “Zimene mawuwa akutanthauza ndi izi: Mene: Mulungu wawerenga masiku a ufumu wanu ndipo wauthetsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

26 Kumasulira kwake kwa mau awa ndi uku: MENE, Mulungu anawerenga ufumu wanu, nautha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Kumasulira kwake kwa mau awa ndi uku: MENE, Mulungu anawerenga ufumu wanu, nautha.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 5:26
11 Mawu Ofanana  

Munthu akafa, kodi adzakhalanso ndi moyo? Masiku anga onse a moyo wovutikawu ndidzadikira mpaka itafika nthawi yomasulidwa.


Taona, Ine ndidzadzutsa Amedi amene safuna siliva ndipo sasangalatsidwa ndi golide, kuti amenyane ndi Ababuloni.


Anthu a mitundu yonse adzamutumikira iyeyo, mwana wake ndi chidzukulu chake mpaka nthawi itakwana yoti dziko lake liwonongedwe. Pamenepo mitundu yambiri ndi mafumu amphamvu adzamugonjetsa.


“Mawu amene analembedwa ndi awa: MENE, MENE, TEKELI, PARASINI.


ine Danieli ndinazindikira powerenga mawu a Yehova opatsidwa kwa mneneri Yeremiya, kuti Yerusalemu adzakhala bwinja kwa zaka 70.


zinaululidwa kuyambira kalekale.’


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa