Danieli 3:30 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ndipo mfumu Nebukadinezara anakweza pa ntchito Sadirake, Mesaki ndi Abedenego mʼchigawo cha Babuloni. Onani mutuwoBuku Lopatulika30 Pamenepo mfumu inakuza Sadrake, Mesaki, ndi Abedenego, m'dera la ku Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Pamenepo mfumu inakuza Sadrake, Mesaki, ndi Abedenego, m'dera la ku Babiloni. Onani mutuwo |