Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 2:24 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Motero Danieli anapita kwa Ariyoki, amene mfumu inamusankha kuti akaphe anthu anzeru a ku Babuloni, ndipo anati kwa iye, “Musaphe anthu anzeru a ku Babuloni. Ndiperekezeni kwa mfumu, ndipo ndidzayimasulira maloto ake.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

24 Potero Daniele analowa kwa Ariyoki amene mfumu idamuika aononge eni nzeru a ku Babiloni; anamuka, natero naye, Usaononga eni nzeru a ku Babiloni, undilowetse kwa mfumu, ndipo ndidzaululira mfumu kumasulirako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Potero Daniele analowa kwa Ariyoki amene mfumu idamuika aononge eni nzeru a ku Babiloni; anamuka, natero naye, Usaononga eni nzeru a ku Babiloni, undilowetse kwa mfumu, ndipo ndidzaululira mfumu kumasulirako.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 2:24
3 Mawu Ofanana  

“Maloto aja ndi amenewa; tidzafotokoza tanthauzo lake kwa mfumu.


ndipo iyeyu anati, ‘Usachite mantha, Paulo. Ukuyenera kukayima pamaso pa Kaisara; ndipo Mulungu mwa kukoma mtima kwake wakupatsa miyoyo ya anthu onse amene ukuyenda nawo.’


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa