Danieli 2:13 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Choncho lamulo linaperekedwa kuti anthu anzeru aphedwe, ndipo anatuma anthu kukafunafuna Danieli ndi anzake kuti iwonso aphedwe. Onani mutuwoBuku Lopatulika13 M'mwemo chilamulirocho chidamveka, ndi eni nzeru adati aphedwe; anafunafunanso Daniele ndi anzake aphedwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 M'mwemo chilamulirocho chidamveka, ndi eni nzeru adati aphedwe; anafunafunanso Daniele ndi anzake aphedwe. Onani mutuwo |