Danieli 11:22 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kenaka adzagonetsa gulu lalikulu lankhondo kuphatikizapo Mkulu wa Ansembe wapangano. Onani mutuwoBuku Lopatulika22 Ndipo mwa mayendedwe ake a chigumula adzakokololedwa pamaso pake, nadzathyoledwa, ngakhale kalonga yemwe wa chipangano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo mwa mayendedwe ake a chigumula adzakokololedwa pamaso pake, nadzathyoledwa, ngakhale kalonga yemwe wa chipangano. Onani mutuwo |