Danieli 10:18 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kenaka wooneka ngati munthu uja anandikhudzanso ndipo anandipatsa mphamvu. Onani mutuwoBuku Lopatulika18 Pamenepo anandikhudzanso wina, maonekedwe ake ngati munthu, nandilimbikitsa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pamenepo anandikhudzanso wina, maonekedwe ake ngati munthu, nandilimbikitsa ine. Onani mutuwo |