Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Afilipi 4:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ndikudandaulira Euodiya ndi Suntuke kuti akhale ndi mtima umodzi mwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Ndidandaulira Yuwodiya, ndidandaulira Sintike, alingirire ndi mtima umodzi mwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndidandaulira Yuwodiya, ndidandaulira Sintike, alingirire ndi mtima umodzi mwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Yuwodiyayo ndi Sintikeyo ndaŵapemba, chonde akhale omvana, popeza kuti ndi abale mwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani




Afilipi 4:2
12 Mawu Ofanana  

Kenaka anawalola abale ake aja kuti azipita, ndipo akunyamuka, iye anawawuza kuti, “Osakangana mʼnjira!”


“Mchere ndi wabwino, koma ngati utasukuluka, mungawukoleretsenso bwanji? Mukhale nawo mchere mwa inu nokha, ndipo mukhale pa mtendere wina ndi mnzake.”


Ndidandaulira inu, abale, mʼdzina la Ambuye athu Yesu Khristu kuti nonsenu muvomerezane wina ndi mnzake kuti pasakhale kugawikana pakati panu ndi kuti mukhale amodzi kwenikweni mu nzeru ndi mʼmaganizo.


Tiyeni ife tizikhala mogwirizana ndi zimene tinapeza kale basi.


Muziwachitira ulemu kwambiri mwachikondi chifukwa cha ntchito yawo. Mukhale pa mtendere wina ndi mnzake.


Yesetsani kukhala pa mtendere ndi anthu onse ndi kukhala oyera mtima, pakuti popanda chiyero palibe ndi mmodzi yemwe adzaona Ambuye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa