Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 6:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Atafika pa malo opunthira tirigu a Nakoni, Uza anatambalitsa dzanja lake kuti agwire Bokosi la Mulungu, chifukwa ngʼombe zinkafuna kugwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Ndipo pofika iwo ku dwale la Nakoni, Uza anatambasula dzanja lake, nachirikiza likasa la Mulungu; chifukwa ng'ombe zikadapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo pofika iwo ku dwale la Nakoni, Uza anatambasula dzanja lake, nachirikiza likasa la Mulungu; chifukwa ng'ombe zikadapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Ndipo atafika pa malo opunthirapo tirigu ku Nakoni, ng'ombe zidaafuna kugwa, ndiye Uza nkutambalitsa dzanja kuti agwirire Bokosi la Mulungu lija, naligwiradi.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 6:6
5 Mawu Ofanana  

Atafika pa Goreni ha-Atadi, pafupi ndi Yorodani, anachita mwambo waukulu wa maliro. Choncho Yosefe analira maliro a abambo ake masiku asanu ndi awiri.


Atafika pa malo opunthira tirigu ku Kidoni, Uza anatambalitsa dzanja lake kuti agwire bokosilo, chifukwa ngʼombe zinkafuna kugwa.


“Aaroni ndi ana ake aamuna akamaliza kukutira ziwiya za ku malo wopatulika ndi zipangizo zopatulika zonse, ndipo akakonzeka kusamuka pamalopo, Akohati abwere kudzazinyamula koma asagwire zinthu zopatulikazo. Akatero adzafa. Izi ndizo zinthu zimene Akohati ayenera kunyamula mu tenti ya msonkhano.


“Onetsetsani kuti mabanja a fuko la Kohati asachotsedwe kwa Alevi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa