2 Samueli 5:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Komabe Davide analanda linga la Ziyoni, limene ndi mzinda wa Davide. Onani mutuwoBuku Lopatulika7 Chinkana anatero Davide anathyola linga la Ziyoni, lomwelo ndilo mzinda wa Davide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chinkana anatero Davide anathyola linga la Ziyoni, lomwelo ndilo mudzi wa Davide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Komabe Davide adalanda linga la Ziyoni, ndiye kuti Mzinda wa Davide. Onani mutuwo |
Chipata cha Kasupe chinakonzedwa ndi Saluni mwana wa Koli-Hoze, wolamulira chigawo cha Mizipa. Iye anachimanganso ndi kuyikanso denga ndiponso zitseko, zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iye anakonzanso khoma la Dziwe la Siloamu limene lili pafupi ndi munda wa mfumu mpaka ku makwerero otsikira potuluka mzinda wa Davide.