2 Samueli 5:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Analamulira Yuda ali ku Hebroni kwa zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi, ndipo ali ku Yerusalemu analamulira Israeli yense ndi Yuda kwa zaka 33. Onani mutuwoBuku Lopatulika5 Ku Hebroni anachita ufumu pa Yuda zaka zisanu ndi ziwiri kudza miyezi isanu ndi umodzi; ndi ku Yerusalemu anachita ufumu pa Aisraele onse ndi Ayuda omwe zaka makumi atatu mphambu zitatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ku Hebroni anachita ufumu pa Yuda zaka zisanu ndi ziwiri kudza miyezi isanu ndi umodzi; ndi ku Yerusalemu anachita ufumu pa Aisraele onse ndi Ayuda omwe zaka makumi atatu mphambu zitatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ku Hebroni adalamulira Ayuda zaka zisanu ndi ziŵiri ndi theka. Ndipo ku Yerusalemu adalamulira Israele yense ndi Yuda zaka 33. Onani mutuwo |