2 Samueli 3:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mulungu andilange ine Abineri, andilange kwambiri, ngati sindichitira Davide zimene Yehova anamulonjeza iye mwa lumbiro. Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Mulungu alange Abinere, naonjezepo, ndikapanda kumchitira Davide monga Yehova anamlumbirira; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mulungu alange Abinere, naonjezepo, ndikapanda kumchitira Davide monga Yehova anamlumbirira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Nchifukwa chake Mulungu andilange, ngakhale kundipha kumene, ngati sindimchitira Davide zimene Chauta adamlonjeza. Onani mutuwo |