Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 22:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 “Mafunde a imfa anandizinga; mitsinje yothamanga yachiwonongeko inandiopsa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Pakuti mafunde a imfa anandizinga, mitsinje ya zopanda pake inandiopsa ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pakuti mafunde a imfa anandizinga, mitsinje ya zopanda pake inandiopsa ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 “Zoŵaŵa za imfa zidandizinga, mitsinje ya ku malo a anthu akufa idandisefukira.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 22:5
12 Mawu Ofanana  

Zingwe za imfa zinandizinga; mitsinje yothamanga yachiwonongeko inandiopsa kwambiri.


Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake, nthawi ya usiku nyimbo yake ili nane; pemphero kwa Mulungu wa moyo wanga.


Choncho akadzabwera ngati madzi oyendetsedwa ndi mphepo yamphamvu yamkuntho. Anthu onse kuyambira kumadzulo mpaka kummawa adzaopa dzina la Yehova ndi ulemerero wake.


Munandiponya mʼnyanja yozama, mʼkati mwenimweni mwa nyanja, ndipo madzi oyenda anandizungulira; mafunde anu onse ndi mkokomo wake zinandimiza.


“Mukadzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu ankhondo, inu mudzadziwe kuti kuwonongeka kwake kuli pafupi.


Pamene anthu akunena kuti, “Mtendere ndi chitetezo,” chiwonongeko chidzafika pa iwo mwadzidzidzi, monga zowawa za amayi pobereka, ndipo sadzathawa.


Mmodzi wa angelo asanu ndi awiri aja amene anali ndi mbale zisanu ndi ziwiri anadza nati kwa ine, “Bwera ndikuonetse chilango cha mkazi wadama wotchuka uja amene akukhala pambali pa madzi ambiri.


Kenaka mngeloyo anati kwa ine, “Madzi amene unawaona pamene mkazi wadamayo anakhalapo ndiwo anthu ochuluka, mitundu ndi ziyankhulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa