2 Samueli 19:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ankhondo analowa mu mzinda mwakachetechete tsiku limenelo ngati momwe amalowera anthu mwamanyazi chifukwa athawa ku nkhondo. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo tsiku lija anthu analowa m'mzinda kachetechete, monga azemba anthu akuchita manyazi pakuthawa nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo tsiku lija anthu analowa m'mudzi kachetechete, monga azemba anthu akuchita manyazi pakuthawa nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsiku limenelo anthu adaloŵa mu mzinda kachetechete, monga momwe anthu amaloŵera mu mzinda mwamanyazi, akamathaŵa kunkhondo. Onani mutuwo |