Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 17:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Husai atabwera kwa iye, Abisalomu anati, “Ahitofele wapereka malangizo ake. Kodi tichite zimene wanena? Ngati sichoncho, tiwuze maganizo ako.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Ndipo pakufika Husai kwa Abisalomu, Abisalomuyo ananena naye, Ahitofele analankhula mau akuti; tichite kodi monga mwa kunena kwake? Ngati iai, unene ndiwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo pakufika Husai kwa Abisalomu, Abisalomuyo ananena naye, Ahitofele analankhula mau akuti; tichite kodi monga mwa kunena kwake? Ngati iai, unene ndiwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Husai atabwera kwa Abisalomu, Abisalomuyo adamuuza kuti, “Zimene wanena Ahitofele nzimenezi, kodi tichitedi monga m'mene watilangiziramo? Ngati si choncho, iweyo utiwuze chochita.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 17:6
2 Mawu Ofanana  

Koma Abisalomu anati, “Muyitanenso Husai Mwariki kuti timve zimene iye adzanena.”


Husai anayankha Abisalomu kuti, “Malangizo amene Ahitofele wapereka si abwino pa nthawi ino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa