Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 17:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Malangizo awa anaoneka abwino kwa Abisalomu ndi kwa akuluakulu onse a Israeli.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Ndipo mauwa anamuyenerera Abisalomu, ndi akulu onse a Israele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo mauwa anamuyenerera Abisalomu, ndi akulu onse a Israele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Uphunguwo udakomera Abisalomu ndi atsogoleri onse a Aisraele.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 17:4
8 Mawu Ofanana  

ndipo anthu onse ndidzabwera nawo kwa inu, ngati mkwati amene akubwerera kwa mwamuna wake. Imfa ya munthu mmodzi yekha idzakhalitsa anthu onse pa mtendere.”


Koma Abisalomu anati, “Muyitanenso Husai Mwariki kuti timve zimene iye adzanena.”


Chikonzerochi chinaoneka kuti chinali chabwino kwa mfumu pamodzi ndi anthu onse.


Mfumu ndi nduna zake anakondwera ndi uphungu uwu, kotero mfumu inachita monga momwe ananenera Memukani.


Mkazi wake Zeresi ndi abwenzi ake onse aja anamuwuza kuti, “Anthu apange mtanda wotalika mamita 23 ndipo mmawa upemphe mfumu kuti anthu akhomerepo Mordekai. Kenaka upite ndi mfumu kuphwando mokondwa.” Hamani anakondwera ndi uphungu umenewu ndipo mtanda unapangidwa.


Ngakhale kuti amadziwa chiweruzo cholungama cha Mulungu chakuti amene amachita zinthu zotere amayenera imfa, iwo sangopitiriza chabe zimenezi, koma amavomerezanso amene amazichita zimenezi.


Sauli anayankha kuti, “Yehova akudalitseni pakuti mwandichitira chifundo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa