2 Samueli 15:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenaka Abisalomu amanena kwa iye kuti, “Taona, madandawulo ako ndi abwino ndi oyenera, koma palibe woyimira mfumu woti akumvere.” Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Abisalomu nanena naye, Ona zokamba zako ndizo zabwino ndi zolungama; koma mfumu sinauze wina kuti adzamve za iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Abisalomu nanena naye, Ona zokamba zako ndizo zabwino ndi zolungama; koma mfumu sinauze wina kuti adzamve za iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Abisalomu ankamuuza kuti, “Taona, zimene ukunenazi nzabwino ndi zolungama. Koma mfumu sidaike munthu woti azimva madandaulo anu.” Onani mutuwo |